Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

 

NDIKONDWA kuti
Atate wa M’mwamba,
Atidziwitsa chikondi chakecho;
Ndimaŵerenga m’Uthenga Wabwino,
Kuti Ambuye akonda ana ‘ke.

Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Yesu akonda, andikondabe;
Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Amandikondabe.

Yesu ndim’konda, akondanso ine,
Anandifera pamtanda woopsa;
Wosayenera, woipa ndi
Tsoka langalo Ambuye nachotsa.

Mzimu Woyera akhala mwa ine,
Atsimikiza chikondi cha Yesu:
Ine n’tachimwa amandikumbutsa,
“Lapa mwana we akukonda Yesu.”

Ndikadzawona Ambuye Kumwamba,
Sindidzawopa pokhala akonda:
Anandikonzera kalelo nyumba,
Ndidzakhalamo wokondwa, wokoma.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version