Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 467 NGOLIZO zilira

  1. Home   »  
  2. Hymn 467 NGOLIZO zilira

Hymn 467 NGOLIZO zilira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 467 NGOLIZO zilira

 

NGOLIZO zilira
Za ’mithengawo,
Ndi zipata zonse
Zatsegudwa mbee!
Kristu, Mfumu yathu,
Mbuye wathudi,
Wapambana monse,
Alamulabe.

Ntchito zake zatha,
Timwimbiretu;
Yesuyo wakwera,
Timtamandetu.

’Natipulumutsa
Natiferako,
Ali mfumu ndithu
Kwa Atatewo;
Osasautsidwa,
Osafanso ’yi
Yesu, Mfumu yathu
Adakweradi.

Atipempherera
M’malo ’dalawo,
Tinke kwathu komwe
Ndi chisomocho;
Akonzera malo
Ana akewo;
Yesu alipobe,
Atikondanso.

Post navigation

Previous: Hymn 466 OSANATU, osana,
Next: Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 423 Koma azibvala
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 347 Mfumu iyi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version