Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 467 NGOLIZO zilira

  1. Home   »  
  2. Hymn 467 NGOLIZO zilira

Hymn 467 NGOLIZO zilira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 467 NGOLIZO zilira

 

NGOLIZO zilira
Za ’mithengawo,
Ndi zipata zonse
Zatsegudwa mbee!
Kristu, Mfumu yathu,
Mbuye wathudi,
Wapambana monse,
Alamulabe.

Ntchito zake zatha,
Timwimbiretu;
Yesuyo wakwera,
Timtamandetu.

’Natipulumutsa
Natiferako,
Ali mfumu ndithu
Kwa Atatewo;
Osasautsidwa,
Osafanso ’yi
Yesu, Mfumu yathu
Adakweradi.

Atipempherera
M’malo ’dalawo,
Tinke kwathu komwe
Ndi chisomocho;
Akonzera malo
Ana akewo;
Yesu alipobe,
Atikondanso.

Post navigation

Previous: Hymn 466 OSANATU, osana,
Next: Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version