Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

  1. Home   »  
  2. Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

 

USIKUWO, woyerawo!
Mwana adam’lerayo;
Akakhale Mfumuyo,
Anabadwa m’kholamo,
Mfumu ya mafumu,
Ndi ya anthuwo.

Mwanayo wa Mlunguyo,
Andikonda inetu;
Nan’tayira chumacho,
Nadzagona mu’dzumo,
Ndiyamika Mbuye,
Wanga Yesuyo.

Usikuwo, woyerawo!
Wadzatu mtenderewo;
Ife tonse anthuwo,
Atitenga Mlunguyo,
M’lemekeze “Tate,
Mwana, Mzimunso.

Post navigation

Previous: Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
Next: Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version