Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

 

YEHOVA Mlungu wathu,
Amene mumapatsa
Zipatso za chikondi
Polenga anthu anu,
Mupatse awa ‘ŵiri
Mitima yokondwetsa,
Yofana m’munda muja
Munayendamo kale.

Mbuyathu wokondedwa,
Pokhala m’dziko muno
Munadza ku ukwati,
Naŵadalitsa onse;
Ukwatiwu mukonze,
Mukhale nafe pano;
Iwowa m’ŵadalitse
M’chifundo chanu chonse.

Ndi Mzimutu Woyera
Mufike nayo mphamvu,
Mukatsangane nawo
Akupangana omwe;
Mupatse ’wo chisomo
Chokometsetsa mtima;
Chikuletu chikondi
Chitsazo nchanu chomwe.

Mulungu mwa Atatu,
Atate, Mwana, Mzimu,
Tikhaletu wokondwa
Ndi Inu m’chiyanjano;
Titama Inu Mlungu,
Wokonda ife ndinu;
M’ulendo wathu wonse
Tiyende m’chikondano.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 29 CHIKONDI cha

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version