Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

 

MAWU akewo anamveka ponse,
Olalikidwa ndi aneneriwo;
Kuti yense wakumvera mawuwo,
Apulumuke.

(Mawuwo) Amveke,
(Tu) Kwa onsewo;
(Wo) Muetseratu ‘we sadzafa ndithu.

Tamveratu ‘we Mawu a Mulungu,
Khulupilira mwa
Ambuye Yesu;
Udzalandira moyo wosathawo,
Udzakondwera.

Tsoka kwa iye wosakhulupira,
Zolalikidwa ndi aneneriwo;
Koma patsiku la chiŵeruziro,
Adzafa ndithu

Post navigation

Previous: Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
Next: Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version