Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

 

KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Ndi Iye Mlungu Wamphamvu;
Angelo anapembedza
Mwana wakhanda Iyeyu.

Kamwana kaja ’nayamba
Kuonetsera Atate,
Lero anena Kumwamba:
“Tiana tidze kwa Ine.”

Tibwera ndi tianato
Kukabatiza ’menewa;
Muŵachitire chifundo.
M’ŵapatse Mzimu Woyera.

Angelo anu asunga
Tiana tathu tofoka;
Pa njira yanu tiyenda,
Mulembe m’Mwamba maina.

Mukonda nyimbo za ana,
Kokoma amaimbatu;
Ndi ana athu atama
Atate, Mwana ndi Mzimu.

Post navigation

Previous: Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version