Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

 

MUNDIMVERE, Mbuye wanga
Nkana ine ndimalakwa,
Koma ndinu moyo wanga;
Mbuye, mkhale ndine.

Ndine mlendo pansi pano,
Msanditaye m’dzanja lanu,
Mundisunge mwana wanu;
Mbuye, mkhale ndine.

Munafera ine kale
Kuti mukandimasule,
Lero lino mndinyamule;
Mbuye, mkhale ndine.

Mundidzaze ndi chikondi,
Mndiyeretse m’mtima monse,
Chifuniro changa mthyole;
Mbuye, mkhale ndine.

Imfa ikandifikira,
Inu ndidzakangamira
Ndikaloŵa ine m’mdima,
Mbuye, mkhale ndine.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version