Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

 

MUNDIMVERE, Mbuye wanga
Nkana ine ndimalakwa,
Koma ndinu moyo wanga;
Mbuye, mkhale ndine.

Ndine mlendo pansi pano,
Msanditaye m’dzanja lanu,
Mundisunge mwana wanu;
Mbuye, mkhale ndine.

Munafera ine kale
Kuti mukandimasule,
Lero lino mndinyamule;
Mbuye, mkhale ndine.

Mundidzaze ndi chikondi,
Mndiyeretse m’mtima monse,
Chifuniro changa mthyole;
Mbuye, mkhale ndine.

Imfa ikandifikira,
Inu ndidzakangamira
Ndikaloŵa ine m’mdima,
Mbuye, mkhale ndine.

Post navigation

Previous: Hymn 390 A! YESU, ndapangana
Next: Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version