Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

  1. Home   »  
  2. Hymn 390 A! YESU, ndapangana

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

 

A! YESU, ndapangana
Kutumikira ’Nu
Ndi moyo wanga wonse,
Mbuyanga ndinutu;
Mukhaletu pafupi
Masiku onsewo,
Sindidzaopa konse,
Mutsogolereko.

Ndikufuna kumva Inu,
E, Mawu anuwo,
Ndisamve za satana
Zonyenga zakezo;
Adani anga onse
Andizingiratu;
Mukhaletu pafupi,
Mundithangate ’Nu.

A! Yesu mwapangana
Ndi anthu anuwo
Adzakhala ndinu
Ku Dziko lanulo;
Inenso ndapangana
Ndisabwerere ’yi;
Mndipatse mphamvu yanu
Ambuye ndinudi.

Mundionetse, Yesu,
Mapazi anuwo,
Ndidzapondera awa
Munjira monsemo;
Ndithangateni ine
Ndisalefuke ’yi;
Mundilandire m’Mwamba
Ndikamwaliradi.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version