Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

  1. Home   »  
  2. Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

 

MONGA zomera zonsezo
Zikula ponsepo,
Mulungu mumeretsazo,
Momwemo anawo.

Munali mwana, Yesu ’Nu
Wamng’ono kalelo,
Ndi munakula m’msinkhu ndi
Kutama ’Tatewo.

Ndi ife tinga, mbewuzo
Zomera m’mundawo;
Mumtima mutidyetsedi,
Tikule bwinomo;

Ndi kutsukidwa m’mwazimo
Mumtima mwathu mbee,
Tionetsedwe konseko
A Mlungu ana ’ke.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version