Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

  1. Home   »  
  2. Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

 

MONGA zomera zonsezo
Zikula ponsepo,
Mulungu mumeretsazo,
Momwemo anawo.

Munali mwana, Yesu ’Nu
Wamng’ono kalelo,
Ndi munakula m’msinkhu ndi
Kutama ’Tatewo.

Ndi ife tinga, mbewuzo
Zomera m’mundawo;
Mumtima mutidyetsedi,
Tikule bwinomo;

Ndi kutsukidwa m’mwazimo
Mumtima mwathu mbee,
Tionetsedwe konseko
A Mlungu ana ’ke.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version