Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

 

NDI lokoma m’Mwambamo,
Mbuye, Bwalo lanulo;
Ndi mwabwino muli ’Nu
Dziko losachimwali;
Mtima wana wonsewu
Umakhumba m’Mwambamo
Nkhope ya Mbuyathuyu,
Mlungu wa chisomoyo.

Zimbalame zonsezi
Zimayamikira ’Nu;
Anthu amakondwanso
Okhumbira m’Mwambamo;
Njiŵa yosapumayo
Inafika m’chombocho;
Okhulupirira ’Nu
Amapuma kwanuno.

Anthu opembedzawo
Amakondwa m’mtimamo;
Munapatsa madzitu,
Munagwetsa manawo;
Mumakoma mtimatu
Tidzayamikiratu,
Pachimpando chanucho
Mkhale Mfumu yathudi.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version