Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 364 DZUŴA lapitira,

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

 

DZUŴA lapitira,
Wadza mdimawo,
Mthunzi wamadzulo
Wagwa m’mwambamo.

M’mwambamo nyenyezi
Zithwanima mbee;
Zonse zili m’tulo
Pansi pali duu.

Yesu mutipatse
Tulo toti phee;
Ndi mdalitso wanu
Mndigonetse ’ne

Mpatse ana ’ng’ono
Alotemo mbee;
Anthu aulendo
Msungesungebe.

Mutonthoze mtima
Wopwetekawo;
Akutsata tchimo
Mletse onsewo.

Wonsewu usiku
Andisunge ’ne
Amithenga anu
Akuyera mbee.

Ndidzukanso m’maŵa,
Kucha koti mbuu,
Ndiyeretu mtima
M’maso mwanumo.

Titamadi ’Tate,
Mwana wakeyo,
Mzimu Woyeranso,
Nthaŵinthaŵizo.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version