Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 356 YESU Mbuye onani,

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

 

YESU Mbuye onani,
Tadza poyitana Inu;
M’dzina lanu tifika,
Osekera kwa Atate.
M’khale nafe Inu nokha,
Tikayimba n’kupemphera.

Mbuye, Mzimu Woyera,
Munapatsa ana anu;
Kukalonga mumtima,
Mawu ndipo mvano womwe.
Zinthu zonse pansi pano,
Sizikondweretsa ife.

Mzimu, m’longe m’mtimamo,
Maphunziro achifundo;
Timve lero ndi mawa,
Ndi masiku onse: Yesu!
Ndipo M’mwamba tidzawona,
Tidazimva pansi pano.

Post navigation

Previous: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
Next: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version