Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

  1. Home   »  
  2. Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

 

ATATE, tifika pamaso panu;
Mukomane ndi ife, Mbuye wathu.

Mitima yathu iyi nayo njanu,
Muiyeretse, muikonze Mbuye.

Ndi maso athu awa nawo nganu,
Muŵapenyetse zinthu zanu zokha.

Ndi manja athu awa nawo nganu,
Agwiretu ntchito yanu yokhayo.

Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
Ithamange m’ntchito yanu yokhayo.

Ndi milomo yathu iyinso njanu,
Ilalike Mawu anu kwa onse.

Ndi makutu athu awanso nganu,
Muŵamvetse Mawu anu okhawo.

Tidziperekadi konse kwa Inu
Tikakhale anthu anu okhawo.

Post navigation

Previous: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
Next: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version