Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 345 ATATE, ndipempha

  1. Home   »  
  2. Hymn 345 ATATE, ndipempha

Hymn 345 ATATE, ndipempha

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 345 ATATE, ndipempha

 

ATATE, ndipempha
Tsopano mundimvere,
Ndipempha kuti mundithandize.

Ine ndili munthu
Wochimwa pansi pano,
Munditsuke Mbuye, ndiyeretu.

Ndalema ndathodwa
Ndi zinthu zapadziko,
Zakhalatu goli londimanga.

Yesu Mfumu Inu
Mumandiuza kuti:
“Pemphera, ndipo udzalandira.”

Ndipempha, Ambuye,
Mundidzaze n’chikondi,
Mtima wangawu ukukondeni.

Post navigation

Previous: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
Next: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version