Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 345 ATATE, ndipempha

  1. Home   »  
  2. Hymn 345 ATATE, ndipempha

Hymn 345 ATATE, ndipempha

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 345 ATATE, ndipempha

 

ATATE, ndipempha
Tsopano mundimvere,
Ndipempha kuti mundithandize.

Ine ndili munthu
Wochimwa pansi pano,
Munditsuke Mbuye, ndiyeretu.

Ndalema ndathodwa
Ndi zinthu zapadziko,
Zakhalatu goli londimanga.

Yesu Mfumu Inu
Mumandiuza kuti:
“Pemphera, ndipo udzalandira.”

Ndipempha, Ambuye,
Mundidzaze n’chikondi,
Mtima wangawu ukukondeni.

Post navigation

Previous: Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
Next: Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version