Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

 

AMITHENGA a Mulungu,
Anaimba nyimbo yomwe,
Posonkhana m’mlengalenga,
Natitu usiku womwe;
“Onse azilemekeza
Mlungu Wakumwambamwamba;
Akhalebe ndi mtendere
Anthu ali ponseponse.”

Amithenga anaimba
Ndi usiku m’mlengalenga.

Anamva abusa omwe
Anaŵeta nkhosa zawo.
Mthenga nati:
“Musaope;
Mumve ndikufotokoza:
Wabadwa usiku uno Yesu Kristu Ambuyathu
Ndiye Mpulumutsi wathu;
Anabadwa m’Betlehemu.”

Amithenga anaimba
Ndi usiku m’mlengalenga.

Yesu ndinu Mbuye wathu,
Munasiya za Kumwamba;
Munakhala mwana kuno;
Mnatifera mwaufulu.
Inu nonse amithenga,
Inu mumtamande Iye;
Anthu onse ali pansi Adza akondane naye.

Zoonazi amithenga
Anaimba m’mlengalenga.

Post navigation

Previous: Hymn 33 OWONADI mtima,
Next: Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version