Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

 

KULINSO dziko lowala M’mwamba,
Kunthawi zosatha;
Komwe kulibe mdima bii,
Yesu ndiye nyaliyo.

Mtandawo tidzasenza,
Korona tidzavala,
Pamodzi ndi oyera,
M’dziko la Kumwambako.

Chikondi chake cha Mlengi wathu,
Natuma Yesuyo;
Kudzatifera tonsefe,
Ndikutipatsa moyo.

Mulitu ulemelero M’mwamba,
Kwa anthu omvera;
Omwe akonda Yesuyo,
Ndikugwira ntchitoyo.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version