Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

 

KULINSO dziko lowala M’mwamba,
Kunthawi zosatha;
Komwe kulibe mdima bii,
Yesu ndiye nyaliyo.

Mtandawo tidzasenza,
Korona tidzavala,
Pamodzi ndi oyera,
M’dziko la Kumwambako.

Chikondi chake cha Mlengi wathu,
Natuma Yesuyo;
Kudzatifera tonsefe,
Ndikutipatsa moyo.

Mulitu ulemelero M’mwamba,
Kwa anthu omvera;
Omwe akonda Yesuyo,
Ndikugwira ntchitoyo.

Post navigation

Previous: Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Next: Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hello world!
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version