Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

 

MUMZINDA wa Mulungu
Moyera mulimo,
Ndiye amathu omwe
Olera ifewo;
Mitima yathu yomwe
Ikondwereratu,
Nikhala nawo Mzinda
Wakukongolawu.

Akondwerera anthu Zokoma zonsezi
Za midzi ya padziko
Lapansi lonseli;
Mtendere wake koma
Wa Mzinda wathuwo
Upambanditsa zonse
Zapansi pomwepo.

Ndi nkhondo ikaleka
Kwa Mlungu komweko,
Ndi ukapolo watha,
Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
Ndi zosauka zii!
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Udzoza mutu tho!

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version