Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

  1. Home   »  
  2. Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

 

NDIMAYENDA paulendo
Ndi yaminga njira yake;
Tsoka ndikapeza, koma
Ndinka kwa Atate;
Pena m’mtima mwanga mwada,
Pena andibvuta ‘dani,
Ndikatenga nkhaŵa, mantha,
Amadziŵako.

Ichi chindisangalatsa
M’mene nkhondo indigwira,
M’mene nsoni zazikulu
Zimanditsatira;
Mtima ukhazika m’mene
Kwathu kuja ndikumbuka
Kuti Mlungu ali ndine,
Andisungako.

Mbuye andipeza lero,
Andikonda, andisunga;
Adzapitikitsa mdani
Akamandibvuta.
E, ulendo wanga utha,
Tsono ine ndimwalira;
M’mene ndidzafika kwawo
And’landirako.

Komwe ndi chimwemwe ine
N’dzaonana ndi Atate,
N’dzagwadira ndi kumtama,
Amandikondabe.
Sakandisautsa kanthu
M’dziko lija lakukoma;
Adzandidalitsa Yesu,
Ndidzakondwako.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 163 MALO anachepa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version