Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 308 AULENDO, munka kuti

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

 

AULENDO, munka kuti
Ndi zindodo m’manja mwanu?
Paulendo tizipita;
Aitana Mbuye wathu;
Pamapiri, pamadambo
Tizipita komwe kwawo.
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino,
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino.

Kodi simuopa njira,
Inu anthu akufoka?
Ayi, atiperekeza
Mbuye wathu wotikonda.
Iye amakhala nafe,
Natitsogolera ife.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.

Mundiuze, aulendo,
Muli chiani m’Mwamba muja?
Atibvekako zoyera
Akorona natininkha;
Moyo, moyo atipatsa,
Kwa Mulungu tidzakhala.
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino,
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino.

Kodi inu, aulendo,
Ife titsagane nanu?
Inde, mudze inu nonse,
Mudze nafe paulendo.
Inde, mutiperekeze,
Yesu atilinda ife.
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino,
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version