Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

 

TIYENI, Akristu inu,
Mumenyane nkhondo iyi,
Mukafoka nonse, koma
Yesu akulimbitsani.

Muyendanso kunka komwe,
Mugonjetse mdani wanu;
Musafoke, musaleme,
Musagone konse inu.

Musagonje, anthu inu,
Mtamiretu Yekha Mbuye;
Ipambana mphamvu yake,
Ya Mtsogoli wanu yemwe.

Mtima wanu wonse ndithu
Udzakhala ndi chimwemwe.
Zida zanu mbvale bwino
Zakudzera m’Mwamba momwe.

Limbikani inu nonse,
Msangalalo ngwanu nokha;
Musaope kanthu kena
Mumtamire Mbuye Yekha.

Tiyeni ku nkhondo iyi,
Mugonjetse zonse konko;
Muingitse mdani uja,
Muyendetse m’njira momwemo.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version