Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

 

TIYENI, Akristu inu,
Mumenyane nkhondo iyi,
Mukafoka nonse, koma
Yesu akulimbitsani.

Muyendanso kunka komwe,
Mugonjetse mdani wanu;
Musafoke, musaleme,
Musagone konse inu.

Musagonje, anthu inu,
Mtamiretu Yekha Mbuye;
Ipambana mphamvu yake,
Ya Mtsogoli wanu yemwe.

Mtima wanu wonse ndithu
Udzakhala ndi chimwemwe.
Zida zanu mbvale bwino
Zakudzera m’Mwamba momwe.

Limbikani inu nonse,
Msangalalo ngwanu nokha;
Musaope kanthu kena
Mumtamire Mbuye Yekha.

Tiyeni ku nkhondo iyi,
Mugonjetse zonse konko;
Muingitse mdani uja,
Muyendetse m’njira momwemo.

Post navigation

Previous: Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Next: Hymn 300 AKRISTU limbikani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version