Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

 

IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Zachisautso chomwechili nkudza;
Cha nambala ya a sikisi atatu;
Kodi tidzapiliradi?

Kodi inu mayi mudzapiliradi
Kuyenda inu wausiwa.
Kodi inu bambo mudzapiliradi
Panthawi ya masautsowo?

Zizindikirozo zili kuwoneka,
Kutitu nkhondoyo yayandikadi;
Tisakhaletu odabwitsika konse,
Tilimbike kupemphera.

Tidzawona ena a ifetu zedi,
Tili kudindidwa pamphumi pathu;
Tidziwetu kuti sitinalembedwe,
Mayina m’buku mulibe.

Post navigation

Previous: Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
Next: Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version