Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

 

IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Zachisautso chomwechili nkudza;
Cha nambala ya a sikisi atatu;
Kodi tidzapiliradi?

Kodi inu mayi mudzapiliradi
Kuyenda inu wausiwa.
Kodi inu bambo mudzapiliradi
Panthawi ya masautsowo?

Zizindikirozo zili kuwoneka,
Kutitu nkhondoyo yayandikadi;
Tisakhaletu odabwitsika konse,
Tilimbike kupemphera.

Tidzawona ena a ifetu zedi,
Tili kudindidwa pamphumi pathu;
Tidziwetu kuti sitinalembedwe,
Mayina m’buku mulibe.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version