Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

  1. Home   »  
  2. Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

 

POKONDWA ndi poona vuto
Ndi tsoka pena mwayi,
Ndikumbukira, ndiimbira
Mulungu wangayo.

Kwezani nane Ambuyathu,
Timlemekeze yekha;
Popsinja mtima ndinamtchula,
Nandithangata ’ne

Angelo amazinga nyumba
Za anthu olungama;
Mulungu ateteza omwe
Amkhulupirira.

Laŵani chikondano chake;
Mudzadziŵitsa msanga
Kudala kwawo kwa anake
Omkonda Mbuyeyo.

Opani iye, nimuleke
Kuopa kanthu kena;
Mumtumikire mokondwera,
Akusungani ’nu.

Mulungu wathu Mmodzi yekha
Atate, Mwana, Mzimu,
Akhale ndi ulemerero
Wachikhalirewo!

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version