Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

 

DZIKO lino lapansi,
Moyo ndi wovuta;
Nthawi zina kuseka,
Nthawi zina kulira;
Komatu Ambuye wathu,
Amatisamalira;
Mbale wanga pilira.

Pilira, pilira, mbale wanga pilira,
Dziko lino ndi lovuta
Mbale wanga pilira;
Linadana naye Mwana wa Mulungu,
Mbale wanga pilira.

Zabwino zimabwera,
Ndipo zimapita;
Dziwa kuti Ambuye,
Afunitsa iwedi;
Kuti ugwiretu ntchito,
Yakeyi m’dziko lino;
Mbale wanga pilira.

Tsikulo lilinkudza,
Lomwe Mbuye Yesu;
Adzanena kwa iwe,
Bwera upumuletu;
Kuzovuta ndi zowawa,
Zam’dziko lapansili;
Mbale wanga pilira.

Post navigation

Previous: Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
Next: Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version