Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

 

DZIKO lino lapansi,
Moyo ndi wovuta;
Nthawi zina kuseka,
Nthawi zina kulira;
Komatu Ambuye wathu,
Amatisamalira;
Mbale wanga pilira.

Pilira, pilira, mbale wanga pilira,
Dziko lino ndi lovuta
Mbale wanga pilira;
Linadana naye Mwana wa Mulungu,
Mbale wanga pilira.

Zabwino zimabwera,
Ndipo zimapita;
Dziwa kuti Ambuye,
Afunitsa iwedi;
Kuti ugwiretu ntchito,
Yakeyi m’dziko lino;
Mbale wanga pilira.

Tsikulo lilinkudza,
Lomwe Mbuye Yesu;
Adzanena kwa iwe,
Bwera upumuletu;
Kuzovuta ndi zowawa,
Zam’dziko lapansili;
Mbale wanga pilira.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version