Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 282 INU muli mehere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 282 INU muli mehere,

Hymn 282 INU muli mehere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 282 INU muli mehere,

 

INU muli mehere,
Wa dziko lapansi;
Ukasukuluka,
Sungakolerenso,

Yang’anani bwino,
Muyende m’njirayo;
Kuti mungagwetu,
M’zovuta za dziko.

Pamenepo sungakwanirenso kanthu,
Koma kuti ukaponyedwetu kunja.

Ndinu kuunika,
Kwa dziko lapansi;
Mudzi wapaphiri
Sungabisiketu.

Sungayatse nyali,
N’kuyivundikira;
Koma uyika pachoikapo chake.

Ndipo iwunikira onse
m’nyumbamo;
Chomwecho inu
muunikire dziko.

Kuti pakuwona,
Ntchitozo zabwino;
Alemekezedwe,
Mlungu ‘Tate wanu.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 206 Uzanitu abale,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version