Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version