Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

  1. Home   »  
  2. Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

 

NGATI mtima sumakonda
Yesu supumula bwino;
Mbuye, suwu mtima wanga,
Ndiwo wanu, mulandire.

Dziko lonse ndilitaya;
Ndikondetsa Yesu Mbuye;
An’komera kopambana
Andikondweretsa ndiye.

Ndakudani, mnandikonda
Ndi kukhetsa mwazi wanu.
Simuleka kundikonda;
Ine sindidzalekanso.

Mndisungire mtima wanga,
Uzikhulupira Inu,
Kuti moyo wanga wonse
Ubisaletu mwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version