Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

 

TIMVE za anamwali khumi,
Okonzeka mosiyana;
Asanu anali opusa zedi,
Ena anachenjeradi.

Asanu anatenga mafuta padera,
Iwowa anachenjera,
Asanu sanatenge mafuta adera,
Iwowa anapusadi.

Mkwati pamene anafika,
Pakati pa usikuwo,
Asanu osatenga mafutawo,
Sanathe kulowa m’nyumba.

Tisakhale ngati opusa,
Osatenga mafutawo.
Tikhale ngatitu ochenjerawo,
Titenge mafuta athu.

Mbale ukhale wochenjera,
Pakulapa zoipazo;
Pakukhulupiliratu Mulungu,
Kuti tikalowe M’mwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version