Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 238 MULUNGU wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 238 MULUNGU wanga,

Hymn 238 MULUNGU wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 238 MULUNGU wanga,

 

MULUNGU wanga,
Ndapeza moyo;
Ndili wokondwera
Masiku onse.

Aleluya, muyenera!
Aleluya, Amen.
Aleluya, ndidzamtama
Mulungu wanga.

Mwazi wa Yesu
Unditsukatu,
Ndiye Mbuye wanga
Ndi Mpulumutsi.

Pamtanda wake ’Nafera ine,
Ndi zoipa zanga ’Nazichotsadi.

Mulungu wanga
Andilandira,
Chifukwa cha Yesu
Mwana wakeyo.

Adzabweranso
Kundilandira
Ndikhale ndi Iye
Masiku onse.

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version