Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 238 MULUNGU wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 238 MULUNGU wanga,

Hymn 238 MULUNGU wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 238 MULUNGU wanga,

 

MULUNGU wanga,
Ndapeza moyo;
Ndili wokondwera
Masiku onse.

Aleluya, muyenera!
Aleluya, Amen.
Aleluya, ndidzamtama
Mulungu wanga.

Mwazi wa Yesu
Unditsukatu,
Ndiye Mbuye wanga
Ndi Mpulumutsi.

Pamtanda wake ’Nafera ine,
Ndi zoipa zanga ’Nazichotsadi.

Mulungu wanga
Andilandira,
Chifukwa cha Yesu
Mwana wakeyo.

Adzabweranso
Kundilandira
Ndikhale ndi Iye
Masiku onse.

Post navigation

Previous: Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
Next: Hymn 239 TILI ndi mtendere

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1312 Wina sindifuna ‘yi,
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version