Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

 

AMBUYE, m’imfamo
Munandikonda ine;
Sindikaniza ’Nu
Kanthu konse ’yi.
Ndimagwadira ’nu.
Ndikonda m’mtimamu,
Ndidzaperekatu
Nsembe yangayi.

Kumwamba kwanuko
Mundipempherere;
Ndikhulupirako,
N’dzalandiradi;
Ndisenze mtandawo,
Ndikhale mboniyo,
Ndiperekeko
Mitoloyi.

Ndikhumba mtimawo
Wofatsa ndithu,
Kuti ndiyambe ’ne
Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
Abwere kwawoko,
Inde,kwanutu.

Zambiri zangazo
Mnandipatsa kale,
Ndibweza zonsezi
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikadzaona ’Nu,
Mbuye wabwinotu,
Nsembe yokomatu
Ndidzakhalabe

Post navigation

Previous: Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
Next: Hymn 232 WAFUNAFUNA ine

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version