Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

 

AMBUYE, m’imfamo
Munandikonda ine;
Sindikaniza ’Nu
Kanthu konse ’yi.
Ndimagwadira ’nu.
Ndikonda m’mtimamu,
Ndidzaperekatu
Nsembe yangayi.

Kumwamba kwanuko
Mundipempherere;
Ndikhulupirako,
N’dzalandiradi;
Ndisenze mtandawo,
Ndikhale mboniyo,
Ndiperekeko
Mitoloyi.

Ndikhumba mtimawo
Wofatsa ndithu,
Kuti ndiyambe ’ne
Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
Abwere kwawoko,
Inde,kwanutu.

Zambiri zangazo
Mnandipatsa kale,
Ndibweza zonsezi
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikadzaona ’Nu,
Mbuye wabwinotu,
Nsembe yokomatu
Ndidzakhalabe

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version