Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

 

KUNALI munthu ku Yeriko,
Dzina lake Zakeyu;
Anali munthu wamkulu,
Wokhometsa misonkho.

(M) Kunali Zakeyu,
(O) Ku Yeriko,
(M) Nafunafuna,
(O) Kuwona Yesu,
(M) Koma chifukwa,
(O) Cha khamulo,
Anakwera mumtengo.

Paulendowo Ambuyeyo,
Anafika pamtengo;
Nayang’ana m’mwamba muja,
Anawona Zakeyu,

Ambuye Yesu nanenadi,
“Fulumira nutsike;
Lero lino ndiyenera,
Kukhala m’nyumba mwako.”

Zakoyuyo mofulumira,
Anatsika mumtengo,
Anam’tenga Mbuye Yesu,
Kuti akam’chereze,

Anadandauladi ena,
“Ambuye wachitanji?
Bwanji Iye analowa,
M’nyumba ya wochimwayo?”

Zakeyuyo pakumva ichi,
Anawuza Ambuye:
“Theka la chuma changacho,
Ndidzapatsa osowa.”

Leronso chipulumutsochi,
Chagwera m’nyumba yathu;
Tilape zoipa zathu,
Kutí tipulumuke.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version