Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

  1. Home   »  
  2. Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

 

NDI MISOZI, ndi chisoni,
Ndiliratu kwa Inu Yesu;
Ndi chifundo chandigwira,
Ndilira kutí ndili wanu

E! Kwa Inu, E! Kwa Inu!
Ndilira kuti ndili wanu.

Mbuye Yesu ndi Atate,
Mundiwona ndili wosowa;
Ndimasowa Mzimu wanu,
Kuinga zonse za mumtima.

Mtenderewo, wosanyenga,
Ndilira ine m’mtima mwanga;
Kundimvetsa chimwemwetu,
Ndilira ine m’mtima mwanga.

Kalekale ndinathawa,
Ndinakana kumvera Inu;
Koma lero ndamva kuti,
Muli mwini wake wa moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version