Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

  1. Home   »  
  2. Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

 

NDI MISOZI, ndi chisoni,
Ndiliratu kwa Inu Yesu;
Ndi chifundo chandigwira,
Ndilira kutí ndili wanu

E! Kwa Inu, E! Kwa Inu!
Ndilira kuti ndili wanu.

Mbuye Yesu ndi Atate,
Mundiwona ndili wosowa;
Ndimasowa Mzimu wanu,
Kuinga zonse za mumtima.

Mtenderewo, wosanyenga,
Ndilira ine m’mtima mwanga;
Kundimvetsa chimwemwetu,
Ndilira ine m’mtima mwanga.

Kalekale ndinathawa,
Ndinakana kumvera Inu;
Koma lero ndamva kuti,
Muli mwini wake wa moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
Next: Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version