Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

 

AITANA, aitana dziko lonse,
Imvani mukhaliranji chete?
Aitana,
Aitana aitana dziko lonse.

Mfumu iyi, Mfumu iyi ya Kumwamba
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa anthu onse.
Anthu onse, anthu onse, tinke kwawo.

Aitana,aitana inu mayi,
Ndi Yesu, amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu mayi.

Aitana, aitana inu ’tate,
Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu ’tate.

Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
Zoipa zimene muzichita, muzisiye,
Muzisiye, muzisiye inu nonse.”

Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
Ndi Yesu anatifera ife akuchimwa;
Akuchimwa, akuchimwa tinke kwawo.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version