Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

  1. Home   »  
  2. Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

 

NDICHITENJI kukapeza
Moyo? thandizeni!
Ndili wakutopa; Mzimu,
Muthandize ine.

Zonse zinathedwadi;
Yesu watha zonsezo;
Sutha ntchito, ungomvera
Mawu ake omwewo.

Iye anatsika m’Mwamba,
Anachoka kwawo,
Anafera anthu, nati:
“Ndatha zonse zawo.”

Mbuye wanga ndili kumva,
Ndikondana nanu;
Umapuma mzimu wanga,
Kwathu ndiko kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version