Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

 

PENYETSETSA Yesu,
Mtima wosauka; Anafera iwe,
Idza, nupumule.
Iye anachotsa
Nsoni ndi zoipa;
Penyetsetsa Yesu,
Ndi kukhulupira.

Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa;
Yachuluka ntchito,
Mphamvu idzakula.
Akonzera kwawo
Nyumba zokhalamo;
Penyetsetsa Yesu,
Mtsatetu tsopano.

Penyetsetsa Yesu
Pogwirana nawo;
Nkhondo ikabvuta
Tamva Mbuye wako.
Achuluka’dani,
Iwe ungofoka;
Penyetsetsa Yesu,
Mantha adzachoka.

Ndipo pakuloŵa
M’dziko la Kumwamba,
Udzapeza komwe
Onse adzatama.
Mwa zoŵala zija
Za Kumwamba kwawo,
Udzapenya maso
Yesu Mbuye wako.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version