Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

 

PENYETSETSA Yesu,
Mtima wosauka; Anafera iwe,
Idza, nupumule.
Iye anachotsa
Nsoni ndi zoipa;
Penyetsetsa Yesu,
Ndi kukhulupira.

Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa;
Yachuluka ntchito,
Mphamvu idzakula.
Akonzera kwawo
Nyumba zokhalamo;
Penyetsetsa Yesu,
Mtsatetu tsopano.

Penyetsetsa Yesu
Pogwirana nawo;
Nkhondo ikabvuta
Tamva Mbuye wako.
Achuluka’dani,
Iwe ungofoka;
Penyetsetsa Yesu,
Mantha adzachoka.

Ndipo pakuloŵa
M’dziko la Kumwamba,
Udzapeza komwe
Onse adzatama.
Mwa zoŵala zija
Za Kumwamba kwawo,
Udzapenya maso
Yesu Mbuye wako.

Post navigation

Previous: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
Next: Hymn 163 MALO anachepa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version