Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

 

LERO lino mbale wanga,
Ndilo tsiku lakukoma;
Talandira Mpulumutsi,
Mmene ali kuyitana.

Lero lino mbale wanga,
Usazengereze ayi;
Ngati ulandira Yesu,
Lero, udzachita mwayi.

Lero lino ndi labwino,
Moyo wako uli nawo;
Pena mawa umwalira,
Udzatani mlandu wako?

Lero lino mbale wanga,
Lapa mtima, lapa tchimo;
Yesu adzakulandira,
Ukam’pempha lero lino.

Ndiwe mlendo lero lino,
Myera ndikupempha iwe:
Yesu Mwana wa Mulungu,
Akufuna ndithu iwe.

Inde, lero lino Yesu,
Ayitana inu nonse;
Landirani Mpulumutsi,
Musazengereze konse.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version