Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

 

UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
Inde, moyo tsopanopanotu;
Wolakwira upenye kwa Yesu Mbuyeyo,
Kuwombola naferatu ‘we.

Ona! Ona! Onatu!
Kuli moyo kwa yense
Apenya Yesuyo,
Wakuferatu pamtandapo.

Anasenzapo bwanji uchimo wonsewo,
Ngati wanu pa Yesu sulipo?
Bwanji mwazi wakhetsa kutsuka ifetu,
Ngati uwu sutikwanako?

Zilepheradi zonse kugula moyowo,
Koma mwazi wa Yesu Mbuyeyo;
Khulupi’ra mwamphamvu ya
Mlungu wathuyi,
Kuyeretsa’we m’mtima’komo.

Anatheradi pa mtanda ntchito zonsezi,
Zowombola mizimu yathuyi;
Ndipo yense akadza
Mokondwakondwadi,
Moyo apeza kwa Yesuko.

Post navigation

Previous: Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
Next: Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version