Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

 

MIPINGO iyo idzatu,
Yoyenda mangu pajapo,
Afuma kuti anthuwo?
Afika bwanji komweko?

Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo.”
Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo”

Azizwa anthu ajawo,
Nafunsa, “Ndani mlendoyo?
Wanzeru monga Iyeyo
Kulibe wina konseko.”

Ndi Yesu yemwe kalelo,
’Nakhala munthu pansipa;
Anthenda onsenthaŵiyo
Nachirayake mphamvuyo

Afika Yesu leroli,
Chifundo m’mtima wakemo,
Timfitse msanga kwathuko
Akhale nafe ponsepo.

Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
Timyese Mfumu yathuyo,
Chifukwa tikamkanatu
Tikhala otayikawo.

Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo.
Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo

Post navigation

Previous: Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
Next: Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version