Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

 

MIPINGO iyo idzatu,
Yoyenda mangu pajapo,
Afuma kuti anthuwo?
Afika bwanji komweko?

Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo.”
Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo”

Azizwa anthu ajawo,
Nafunsa, “Ndani mlendoyo?
Wanzeru monga Iyeyo
Kulibe wina konseko.”

Ndi Yesu yemwe kalelo,
’Nakhala munthu pansipa;
Anthenda onsenthaŵiyo
Nachirayake mphamvuyo

Afika Yesu leroli,
Chifundo m’mtima wakemo,
Timfitse msanga kwathuko
Akhale nafe ponsepo.

Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
Timyese Mfumu yathuyo,
Chifukwa tikamkanatu
Tikhala otayikawo.

Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo.
Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version