Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

 

SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
Pali anthu otayika, masiku alikutha;
Ngati tikondwerera,
Pakuyenda ulendowu,
Tonse tidzachita bwino, masiku alikutha.

Akutha, akutha, masiku akutha,
Tonse tichitetu bwino, masiku ali kutha.

Tisakhale awulesi, masiku alikutha,
Nkhope zathu zikondwere, masiku alikutha;
Dziko ili ndi lochimwa, lodzaza ndi chisoni,
Thangatani akugwawo, masiku alikutha.

Tamangidwa ndi unyolo, masiku alikutha,
Tisiyetu zoipazi, masiku alikutha;
Tonsefe muzabwinotu
Tidzakhala ndi Mlungu;
Ndipo tidzakondweradi mu nthawi zamuyaya,

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version