Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

  1. Home   »  
  2. Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

 

MULI ndi ludzu, idzani
Kumadzi amoyo
Imwani monse kolere
Kuchitsime konko.

Munka kangati kulaŵa
Madzi onyengera?
Musataye mphamvu yanu,
Musataye chuma.

Imvani, Yesu akuti;
“Chuma ndili nacho,
Landirani, yemwe amva
Akhale ndi moyo.”

Funani Mlungu tsopano.
Akulindirani;
Iye ndiye wachifundo,
Akulandirani.

Ali wokhululukira;
Imvani ananu:
Mtima wake usiyana
Ndi mitima yathu.

Monga m’Mwamba mupambana
Zonse pansi pano;
Choncho maganizo ake
Apitira athu.

Anthu onse a padziko
Adzamvera Mlungu:
Adzakhala ndi chimwemwe,
Nadzamtama ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version