Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

  1. Home   »  
  2. Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

 

MULI ndi ludzu, idzani
Kumadzi amoyo
Imwani monse kolere
Kuchitsime konko.

Munka kangati kulaŵa
Madzi onyengera?
Musataye mphamvu yanu,
Musataye chuma.

Imvani, Yesu akuti;
“Chuma ndili nacho,
Landirani, yemwe amva
Akhale ndi moyo.”

Funani Mlungu tsopano.
Akulindirani;
Iye ndiye wachifundo,
Akulandirani.

Ali wokhululukira;
Imvani ananu:
Mtima wake usiyana
Ndi mitima yathu.

Monga m’Mwamba mupambana
Zonse pansi pano;
Choncho maganizo ake
Apitira athu.

Anthu onse a padziko
Adzamvera Mlungu:
Adzakhala ndi chimwemwe,
Nadzamtama ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
Next: Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version