Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 112 ELISA mneneri,

  1. Home   »  
  2. Hymn 112 ELISA mneneri,

Hymn 112 ELISA mneneri,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 112 ELISA mneneri,

 

ELISA mneneri,
Wachita zamphamvu;
Kuyandamitsa nkhwangwayo,
Pa Yolodani’po.

(M) Nkhwangwayo,
(O) Ndiyobwereka,
Nalira mnyamatayo;
Popeza ndiyobwereka,
Pa Yolodanipo.

Elisa mneneri,
Natenga kamtengo;
Naponya pamadzi paja,
Nkhwangwa niyandama.

Mulungu wamphamvu,
Natuma Mwana ‘ke;
Kuti atifere ife,
Kutipulumutsa.

Nanga ife lero,
Kodi takonzeka;
Kusiya machimo athu,
Kutsata Yesuyo?

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version