Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 112 ELISA mneneri,

  1. Home   »  
  2. Hymn 112 ELISA mneneri,

Hymn 112 ELISA mneneri,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 112 ELISA mneneri,

 

ELISA mneneri,
Wachita zamphamvu;
Kuyandamitsa nkhwangwayo,
Pa Yolodani’po.

(M) Nkhwangwayo,
(O) Ndiyobwereka,
Nalira mnyamatayo;
Popeza ndiyobwereka,
Pa Yolodanipo.

Elisa mneneri,
Natenga kamtengo;
Naponya pamadzi paja,
Nkhwangwa niyandama.

Mulungu wamphamvu,
Natuma Mwana ‘ke;
Kuti atifere ife,
Kutipulumutsa.

Nanga ife lero,
Kodi takonzeka;
Kusiya machimo athu,
Kutsata Yesuyo?

Post navigation

Previous: Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Next: Hymn 113 KALERO anthu onse

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version