Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

 

MZIMU Woyera, mudzetu,
Tiyeretsedwe m’mtimamu;
Mupatse anthu anuwa
Mitulo yanu yonseyo.

Kudzoza kwa Kumwambako
Kutitonthoza m’mtimamo,
Ndi kutidzutsa m’moyomu,
Tikhale okondanatu.

Pankhope pathu mthirepo
Chisomo chanu chijacho;
Mtendere mutininkhebe,
Mutiyendetse ponse phee!

Tionetseni tonsetu
Umodzi wanu wonsemo,
Atate, Mwana, Mzimu ’Nu
Tiimbe Nthaŵi zonsezo:

Titamire Nthaŵi zonse
’Tate, Mwana, Mzimu, Nonse.
Amen

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version