Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

 

MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
Mufike nazo mphamvu zanu zazikuluzo.

Mufike monga nyali younika m’mtimamo.
Mutidziŵitse zakuipa zakukhalamo.

Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
Mutiyeretse ifetu m’mitima mwathumo.

Mufike monga ngati njiŵa yamtenderewo.
Kutitu anthu anu onse akondanetu.

Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
Tikhale tonse nazo mphamvu zanu zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version