Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

 

OYAMIKA Mlungu m’bwere,
Zamasika mudzayimbe;
Dzinthu dzathu takolola,
Sidzionongeka m’minda.
Mlungu Mlengi asamala,
Zotisowa akonzera;
M’lowe m’nyumba ya Chauta.
M’kweze nyimbo zamasika.

Dziko lonse n’la Mulungu,
Kuti lim’balire dzinthu;
M’munda zonse zimamera,
Zakukoma ndi zoipa.
Mmera udza, bwino ngala,
Maso omwe amakhwima;
Mutilole, mwini dzinthu,
Tikakhale dzinthu dzanu.

Adzabwera Mbuye wathu,
Kukolola dzinthu dzake;
M’munda mwake akachotse,
Minga ndi zoipa zonse.
Adzatumanso angelo,
Minga akaponye m’moto;
Koma tirigu amsunge,
M’nkhokwe yake nthawi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version