Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

  1. Home   »  
  2. Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

 

MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
Ndi mtima wokondwera kuloŵa m’nyumbayi;
Chifukwa cha zabwino mwatichitirazi
Tikukuyamikirani leroli.

Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
Mwatimangira ’fe kuno kachisi wanuyu!
Ndi ulemerero wanu mudzaze m’nyumbayi;
Muyeretse, mudalitse munomu.

Tikondwa tonse ndikukuthokozani ’Nu
Poyamba kupemphera ndikuimbira ’mu;
Mommuno nsiku zonse mukhale nafetu,
Monga ndi angelo anu m’Mwambamo.

Ikhale ngati nyali yoŵala nyumbayi,
Yakutsogoza onse ophunthwa m’mdima bii;
Akunja ndi Akristu m’ŵapulumutse ndi
Kuunika kotuluka munomu.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version