Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

  1. Home   »  
  2. Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

 

MBUYE mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Utsani anthu akufa
Ndi mawu a mphamvu.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Tauzirani pa ife
Ndi mweya wa Mzimu

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’mitimamo!
Mumvetse njala kwa Inu—
Mutikhutitsenso.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’kati mwa anthu!
Chikondi chawo chikule
Muchikolezetu.

Mbuye mtsitsimutse!
Mawu alimbike,
Pamene aphunzitsidwa
Onsewa amvere!

Mbuye mtsitsimutse!
Mzimu adzazetu!
Kwa ife kudzakhala mwayi,
Kwa Inu ulemu.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version