Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

  1. Home   »  
  2. Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

 

MBUYE mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Utsani anthu akufa
Ndi mawu a mphamvu.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Tauzirani pa ife
Ndi mweya wa Mzimu

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’mitimamo!
Mumvetse njala kwa Inu—
Mutikhutitsenso.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’kati mwa anthu!
Chikondi chawo chikule
Muchikolezetu.

Mbuye mtsitsimutse!
Mawu alimbike,
Pamene aphunzitsidwa
Onsewa amvere!

Mbuye mtsitsimutse!
Mzimu adzazetu!
Kwa ife kudzakhala mwayi,
Kwa Inu ulemu.

Post navigation

Previous: Hymn 427 AULENDO amayenda
Next: Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version