Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

 

DZIKO lonse lapansi,
Linachimwa kwa Mlungu,
Chilango chake ndicho cha imfa;
Koma podza Yesuyo,
Anathetsa mlanduwo;
Potifera ife pamtandapo.

Onani,
Mwana wa Nkhosa,
Wachotsa tchimo lonse pansipa;
Ndiye Yesu Mfumuyo,
Ndiye Mpulumutsiyo;
Wotifera ife pamtandapo.

Tsono mmene tadziwa,
Kuti ndife ochimwa,
Tiyeni tinke kwa Ambuyewo;
Tisachite manyazi,
Tiwauze tchimolo;
Iwo adzatikhululukira.

Wotikhululukira,
Adzatiwuza tonse,
Kuti tisadzachimwenso ndithu;
Zakale zatha ndithu,
Zatsala zatsopano;
Tasamba mwazi wake tayera.

Post navigation

Previous: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
Next: Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version