Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

 

DZIKO lonse lapansi,
Linachimwa kwa Mlungu,
Chilango chake ndicho cha imfa;
Koma podza Yesuyo,
Anathetsa mlanduwo;
Potifera ife pamtandapo.

Onani,
Mwana wa Nkhosa,
Wachotsa tchimo lonse pansipa;
Ndiye Yesu Mfumuyo,
Ndiye Mpulumutsiyo;
Wotifera ife pamtandapo.

Tsono mmene tadziwa,
Kuti ndife ochimwa,
Tiyeni tinke kwa Ambuyewo;
Tisachite manyazi,
Tiwauze tchimolo;
Iwo adzatikhululukira.

Wotikhululukira,
Adzatiwuza tonse,
Kuti tisadzachimwenso ndithu;
Zakale zatha ndithu,
Zatsala zatsopano;
Tasamba mwazi wake tayera.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version