Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

  1. Home   »  
  2. Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

 

POKONDWA ndi poona vuto
Ndi tsoka pena mwayi,
Ndikumbukira, ndiimbira
Mulungu wangayo.

Kwezani nane Ambuyathu,
Timlemekeze yekha;
Popsinja mtima ndinamtchula,
Nandithangata ’ne

Angelo amazinga nyumba
Za anthu olungama;
Mulungu ateteza omwe
Amkhulupirira.

Laŵani chikondano chake;
Mudzadziŵitsa msanga
Kudala kwawo kwa anake
Omkonda Mbuyeyo.

Opani iye, nimuleke
Kuopa kanthu kena;
Mumtumikire mokondwera,
Akusungani ’nu.

Mulungu wathu Mmodzi yekha
Atate, Mwana, Mzimu,
Akhale ndi ulemerero
Wachikhalirewo!

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version