Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

  1. Home   »  
  2. Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

 

POKONDWA ndi poona vuto
Ndi tsoka pena mwayi,
Ndikumbukira, ndiimbira
Mulungu wangayo.

Kwezani nane Ambuyathu,
Timlemekeze yekha;
Popsinja mtima ndinamtchula,
Nandithangata ’ne

Angelo amazinga nyumba
Za anthu olungama;
Mulungu ateteza omwe
Amkhulupirira.

Laŵani chikondano chake;
Mudzadziŵitsa msanga
Kudala kwawo kwa anake
Omkonda Mbuyeyo.

Opani iye, nimuleke
Kuopa kanthu kena;
Mumtumikire mokondwera,
Akusungani ’nu.

Mulungu wathu Mmodzi yekha
Atate, Mwana, Mzimu,
Akhale ndi ulemerero
Wachikhalirewo!

Post navigation

Previous: Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
Next: Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version