Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 282 INU muli mehere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 282 INU muli mehere,

Hymn 282 INU muli mehere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 282 INU muli mehere,

 

INU muli mehere,
Wa dziko lapansi;
Ukasukuluka,
Sungakolerenso,

Yang’anani bwino,
Muyende m’njirayo;
Kuti mungagwetu,
M’zovuta za dziko.

Pamenepo sungakwanirenso kanthu,
Koma kuti ukaponyedwetu kunja.

Ndinu kuunika,
Kwa dziko lapansi;
Mudzi wapaphiri
Sungabisiketu.

Sungayatse nyali,
N’kuyivundikira;
Koma uyika pachoikapo chake.

Ndipo iwunikira onse
m’nyumbamo;
Chomwecho inu
muunikire dziko.

Kuti pakuwona,
Ntchitozo zabwino;
Alemekezedwe,
Mlungu ‘Tate wanu.

Post navigation

Previous: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
Next: Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version