Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 282 INU muli mehere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 282 INU muli mehere,

Hymn 282 INU muli mehere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 282 INU muli mehere,

 

INU muli mehere,
Wa dziko lapansi;
Ukasukuluka,
Sungakolerenso,

Yang’anani bwino,
Muyende m’njirayo;
Kuti mungagwetu,
M’zovuta za dziko.

Pamenepo sungakwanirenso kanthu,
Koma kuti ukaponyedwetu kunja.

Ndinu kuunika,
Kwa dziko lapansi;
Mudzi wapaphiri
Sungabisiketu.

Sungayatse nyali,
N’kuyivundikira;
Koma uyika pachoikapo chake.

Ndipo iwunikira onse
m’nyumbamo;
Chomwecho inu
muunikire dziko.

Kuti pakuwona,
Ntchitozo zabwino;
Alemekezedwe,
Mlungu ‘Tate wanu.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version