Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

  1. Home   »  
  2. Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

 

MBUYE ndamva mwawazira
Anthu ena madalitso;
Mvula yanu yawagwera;
Mbuye, ine mudalitse.

Etu ine, etu ine,
Mbuye, ine mudalitse.

’Tate, msandipitirire,
Ndimaipa mtima ine;
Ndiyenera munditaye,
Koma mukhululukire.

Yesu, msandipitirire
Kuti ndinu ndikondane;
Ndinalira Inu Mbuye,
Msandileke poitana.

Mzimu, msandipitirire,
Mupenyetsatu akhungu
Mboniyo ya Mbuye Yesu,
Mundipatse ine mphamvu.

Ndinagona mwa zoipa,
Ndinakunyozani ine,
Dziko lino ndinakonda,
Mbuye, mukhululukire.

Ha! chikondi cha Mulungu,
Mwazi wa Mbuyathu Yesu,
Chiyanjano cha Mzimuyo
Zonse zidzalemekeza.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version