Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

  1. Home   »  
  2. Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

 

MBUYE ndamva mwawazira
Anthu ena madalitso;
Mvula yanu yawagwera;
Mbuye, ine mudalitse.

Etu ine, etu ine,
Mbuye, ine mudalitse.

’Tate, msandipitirire,
Ndimaipa mtima ine;
Ndiyenera munditaye,
Koma mukhululukire.

Yesu, msandipitirire
Kuti ndinu ndikondane;
Ndinalira Inu Mbuye,
Msandileke poitana.

Mzimu, msandipitirire,
Mupenyetsatu akhungu
Mboniyo ya Mbuye Yesu,
Mundipatse ine mphamvu.

Ndinagona mwa zoipa,
Ndinakunyozani ine,
Dziko lino ndinakonda,
Mbuye, mukhululukire.

Ha! chikondi cha Mulungu,
Mwazi wa Mbuyathu Yesu,
Chiyanjano cha Mzimuyo
Zonse zidzalemekeza.

Post navigation

Previous: Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
Next: Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version