Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 254 PAMENE ndisawuka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 254 PAMENE ndisawuka,

Hymn 254 PAMENE ndisawuka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 254 PAMENE ndisawuka,

 

PAMENE ndisawuka,
Pamene ndivutidwa;
Mizimu yakuipa,
Ikadza nindiyesa.

Mulungu wanga,
Mwini mphamvu;
M’kandikumbukire ‘ne.

Pamene ndilemedwa,
Ndi zakuipa zanga;
Polowa mdima m’mtima,
Pochita ine mantha.

Masiku anga onse,
Mulungu mundisunge;
Pamene ndimwalira,
Ndi tsiku lomaliza.

Post navigation

Previous: Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
Next: Hymn 255 KHALA chete mtima wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version